Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Anzanu

Kupeza anzako apamtima kungakhale kovuta, koma kupitiriza kukhala nawo kungakhalenso kovuta kwambiri. Mungatani kuti mupeze komanso mupitirize kukhala ndi anzanu abwino?

Making and Keeping Friends

Kulimbana ndi Vuto Losowa Ocheza Nawo

Kodi mumasowa anthu ocheza nawo? Gwiritsani ntchito mafunsowa kuti mudziwe chimene chimapangitsa kuti muzisowa anthu ocheza nawo komanso zimene mungachite kuti muthane ndi vutoli.

Kuonjezera Anzanga

Onani zimene mungachite kuti muthe kuonjezera anzanu komanso chifukwa chake.

Musamapitirire Malire

Muzitumiza mameseji oyenera kwa anzanu amene si amuna kapena akazi anu.

Challenges

Musamangotengera Zochita za Anzanu

Zinthu 4 zimene zingakuthandizeni kuti muzisankha nokha zochita mwanzeru.

Ndingatani Kuti Ndikonze Zomwe Ndinalakwitsa M’mbuyo?

Musaganize kuti kukonza zomwe munalakwitsa n’kovuta kwambiri.

Kodi Ndingatani Kuti Ndithetse Miseche?

Ngati anzanu ayamba kulankhula zonyoza kapena zoipa za anthu ena, musayankhire nawo koma sinthani nkhaniyo!

Kodi N’kungocheza Kapena Kukopana?

Nkhani imene munthu wina angaione ngati yocheza, wina angaione ngati yomukopa. Mungatani kuti muzipewa kutumiza mameseji olakwika?