Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Banja

Kodi zikukuvutani kugwirizana ndi makolo anu? Kodi simumagwirizana kwenikweni ndi abale anu? Baibulo lingakuthandizeni kuthana ndi mavuto amenewa komanso mavuto ena amene mabanja amakumana nawo.

Relationship With Parents

Kodi Ndingatani Kuti Ndizilankhulana Bwino ndi Makolo Anga?

Kodi mungatani kuti mulankhulane ndi makolo anu pamene mukuona ngati simufuna kulankhula?

Kuganizira za Malamulo

Ganizirani bwino za malamulo omwe mumaona kuti ndi ovuta.

Kodi Ndingatani Kuti Makolo Anga Azindilolako Kuchita Zinthu Zina?

Mukhoza kuganiza kuti makolo anu akuyenera kumakuonani kuti ndinu munthu wamkulu, koma iwo sangagwirizane ndi maganizo amenewa. Kodi mungachite zinthu ziti kuti makolo anu ayambe kukukhulupirirani?

Ngati Bambo Kapena Mayi Anu Akudwala

Mfundo za patsambali zingakuthandizeni posamalira bambo kapena mayi anu amene akudwala matenda aakulu komanso podzisamalira nokha.

Home Life

Zimene Mungachite Mukasemphana Maganizo ndi Abale Anu

Gwiritsani ntchito tsambali kuti mumvetse bwino zimene zachitika komanso kuti muyambirenso kugwirizana ndi abale anu.

Kodi Nthawi Zina Mumasowa Mpata Wochitira Zinthu Panokha?

Onani zimene mungachite kuti makolo anu azikudalirani.