Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Moyo Wauzimu

Nthawi zina sizikhala zophweka kutsatira mfundo za m’Baibulo, koma kuzitsatira kumathandiza kuti zinthu zizikuyenderani bwino pa moyo wanu. Kodi zimenezi zingatheke bwanji?

Belief in God

Achinyamata Ena Akufotokoza Zokhudza Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu

M’vidiyo ya maminitsi atatuyi, achinyamata akufotokoza chifukwa chake amakhulupirira kuti kuli Mulungu.

Kodi N’zomveka Kukhulupirira Kuti Mulungu Alipo?

Onani achinyamata awiri amene anapeza mayankho a mafunso awo n’kulimbitsa chikhulupiriro chawo.

Zifukwa Zokhalira ndi Chikhulupiriro—Kodi Zinangokhalapo Zokha Kapena Zinachita Kulengedwa?

Fabian ndi Marith akufotokoza zomwe zinachititsa kuti chikhulupiriro chawo chikhalebe cholimba atauzidwa kuti zinthu zinachita kusintha kusukulu.

N’chifukwa Chiyani Ndimakhulupirira Zoti Kuli Mulungu?

Khalani okonzeka kuti muzitha kufotokoza zimene mumakhulupirira koma mwaulemu, mopanda mantha komanso mosadandaula.

How to Draw Close to God

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupemphera?

Kodi pemphero limangothandiza kuti maganizo akhale m’malo, kapena limathandizanso m’njira zina?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupezeka Pamisonkhano ya pa Nyumba ya Ufumu?

Mlungu uliwonse a Mboni za Yehova amakumana kawiri pa nyumba yomwe amalambirira yotchedwa Nyumba ya Ufumu. Kodi kumeneko kumachitika zotani, nanga mungapindule bwanji ngati mutapezeka pamisonkhano yawo?

Reading and Studying the Bible

Achinyamata Akukambirana Zokhudza Kuwerenga Baibulo

Kuwerenga sikophweka, koma kuwerenga Baibulo n’kothandiza kwambiri. Achinyamata anayi akufotokoza mmene kuwerenga Baibulo kwawathandizira.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?

Yankho la funso limeneli lingakuthandizeni kuti muzisangalala kwambiri pa moyo wanu.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 1: Kuganizira Mozama Mfundo za M’baibulo

Tiyerekeze kuti mwaona chikwama cha ndalama chomwe chikuoneka kuti ndi chakalekale, kodi simungakhale ndi chidwi kuti muone zimene zili mkatimo? Baibulo lili ngati chikwama choterocho. Mumapezeka mfundo zambiri zothandiza.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 2: Zimene Mungachite Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzikusangalatsani

Zinthu 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muziona zimene mukuwerenga m’Baibulo kuti ndi zenizeni.

Growing Spiritually

Ndingatani Kuti Ndikonze Zomwe Ndinalakwitsa M’mbuyo?

Musaganize kuti kukonza zomwe munalakwitsa n’kovuta kwambiri.

Cameron Anapeza Moyo Wabwino Kwambiri

Kodi mukufuna kukhala munthu wosangalala? Mvetserani pamene Cameron akufotokoza zimene zinamuthandiza kuti akhale wosangalala atapita kumalo amene samaganizira kuti angafikeko.