Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Mtendere wa M’maganizo

Achinyamata ambiri amavutika ndi nkhawa, matenda amaganizo, kudziona kuti ali okhaokha ndiponso amatopa kwambiri. Onani zimene zingakuthandizeni kukhala ndi mtendere wa m’maganizo.

Negative Emotions

Kulimbana ndi Vuto la Mmene Mukumvera Mumtima

Zoti muchitezi zikuthandizani kuti mudziwe zimene mungachite mukamakumana ndi mavuto.

Zimene Mungachite Mukakhumudwa

Kodi n’chiyani chimene chingakuthandizeni kukhala wosangalala mukakhumudwa?

Zimene Mungachite Kuti Muyambirenso Kusangalala

Kodi mungatani ngati mukukhalabe okhumudwa kwa nthawi yaitali?

Zomwe Zingakuthandize Kuti Usamayembekezere Kuchita Zinthu Mosalakwitsa Chilichonse

Zoti muchitezi zikuthandizani kukhala ndi maganizo oyenera a zimene anthu ena komanso inuyo mungakwanitse kuchita.

Challenges

Ndingatani Ngati Anzanga Amandivutitsa?

Simungathe kuchititsa kuti anthu asamakuvutitseni, koma mungathe kusintha mmene mumawayankhira.

Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani?

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe chifukwa chake anthu amavutitsa anzawo komanso zimene mungachite kuti asiye kukuvutitsani.

Zimene Mungachite Kuti Anthu Asiye Kukuvutitsani pa Intaneti

Tsambali likuthandizani kuzindikira ubwino ndi mavuto a njira zosiyanasiyana komanso kuti muthe kudziwa zoyenera kuchita kuti winawake asamakuvutitseni pa Intaneti.

Zomwe Zingakuthandizeni Ngati Chibwenzi Chatha

Mfundo zomwe zili mu zochitazi zikuthandizani kuti muzisangalalabe ngakhale kuti chibwenzi chatha.