Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Thanzi Lanu

Onani zomwe mungachite kuti mukhale ndi thanzi labwino kapenanso kuti mupirire matenda ovuta. Kaya zinthu zili bwanji pa moyo wanu, Baibulo lili ndi malangizo omwe angakuthandizeni kwambiri.

Health Threats

Kodi Mungatani pa Nkhani ya Mowa?

Zoti muchitezi zikuthandizani kudziwa zoyenera kuchita ngati anzanu akukukakamizani kuti mumwe mowa.

Ganizirani Zimene Zingachitike Ngati Mutamwa Mowa

Kuchita zinthu chifukwa cha mowa, anthu ambiri amanena kapena kuchita zinthu zimene pambuyo pake amanong’oneza nazo bondo. Kodi mungatani kuti mupewe mavuto amene amakhalapo chifukwa chomwa kwambiri mowa?

Musawononge Moyo Wanu Chifukwa cha Kusuta

Anthu ambiri amasuta kapena kuvepa. Komabe ena asiya ndipo enanso akufunitsitsa kusiya. N’chifukwa chiyani akuchita zimenezi? Kodi kusuta kungawonongedi moyo wanu?