Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Zokhudza Inuyo

Kodi inuyo ndi ndani? Nanga mumayendera mfundo zotani? Ngati mungadzidziwe bwino, zingakuthandizeni kuti muzisankha nokha zochita m’malo moti anthu ena azikusankhirani.

My Character

Kodi Ndili pa Ubwenzi ndi Yehova?

Kudziwa yankho la funsoli kungakuthandizeni kuthana ndi mavuto amene mukukumana nawo.

Kodi Ndinu Woona Mtima?

Dzifufuzeni pogwiritsa ntchito mafunso atatuwa.

Zomwe Zingakuthandize Kuti Usamayembekezere Kuchita Zinthu Mosalakwitsa Chilichonse

Zoti muchitezi zikuthandizani kukhala ndi maganizo oyenera a zimene anthu ena komanso inuyo mungakwanitse kuchita.

Musamangotengera Zochita za Anzanu

Zinthu 4 zimene zingakuthandizeni kuti muzisankha nokha zochita mwanzeru.

Mmene Mungasankhire Munthu Womutsanzira

Gawoli likuthandizani kuti mudziwe amene mungamutsanzire.

My Actions

Zimene Mungachite Kuti Muthandize Ena

Mukhoza kuthandiza anthu amene mumakhala nawo pafupi. Nkhani ino ili ndi njira zitatu zimene mungatsatire pokonza mapulani oti muthandize ena.

My Appearance

Zovala Zimene Ndimakonda Kuvala

Pepalali lili ndi mfundo zimene zingakuthandizeni kuti muzivala zovala zoyenera.

Zimene Achinyamata Amanena pa Nkhani ya Maonekedwe

N’chifukwa chiyani achinyamata ambiri zimawavuta kuti azisangalala ndi mmene amaonekera? N’chiyani chingawathandize pa nkhaniyi?