Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

MAKADI A ANTHU OTCHULIDWA M’BAIBULO

Rahabi

Pangani dawunilodi khadi la munthu wotchulidwa m’Baibuloli kuti muphunzire zambiri za Rahabi, yemwe analimba mtima n’kubisa azondi awiri ochokera ku Isiraeli. Sindikizani, dulani, pindani pakati ndi kusunga.