Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo

Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo

Kodi inuyo mukhoza kukhala aukhondo komanso oyera ngati Yehova? Kalebe anatengera chitsanzo cha Yehova pa nkhani imeneyi.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.