Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo
Kodi inuyo mukhoza kukhala aukhondo komanso oyera ngati Yehova? Kalebe anatengera chitsanzo cha Yehova pa nkhani imeneyi.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.