Posita: Ndi Ndani Angakhale Mnzanga?
Positayi ingakukumbutseni kufunika kosankha anzanu omwe amakonda Yehova.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.