Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Yehova ndi Mnzanga Wapamtima

Yehova ndi Mnzanga Wapamtima

Yehova anapanga zinthu zokongola kuti anthufe tizisangalala chifukwa chakuti iye ndi Mnzathu. Kodi ungatchule zina mwa zinthu zomwe anapanga?

 

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.