Banja
Zimene Zingakuthandizeni Kuti Muzisangalala
Muzidalira Kwambiri Mulungu
Kudzifunsa mafunso awiri okha kungathandize kuti banja lanu liziyenda bwino.
Nzeru Zothandiza Kukhala Ndi Banja Losangalala
Kodi amuna, akazi, makolo komanso ana angatani kuti azisangalala m’banja?
Kuti Banja Liziyenda Bwino—Kuchita Zinthu Mogwirizana
Kodi inuyo ndi mwamuna kapena mkazi wanu mumangokhala ngati anthu okhalira limodzi basi?
Mungatani Kuti Banja Lanu Lizisangalala: Muzisonyezana Ulemu
Baibulo lingakuthandizeni kuti muyambe kulemekezana m’banja lanu ngakhale kuti poyamba simunkalemekezana.
Muzikhala Okhulupirika
Kuti munthu akhale wokhulupirika m’banja ayenera kupewa chigololo komanso zinthu zina.
Mavuto Komanso Njira Zowathetsera
Zimene Mungachite Kuti Muzigwirizana ndi Achibale
N’zotheka kulemekeza makolo anu popanda kusokoneza banja lanu.
Kuti Banja Liziyenda Bwino—Kukhululukirana
Kodi mungatani kuti musamaganizire kwambiri zimene mwamuna kapena mkazi wanu amalakwitsa?
Mukakumana ndi Mavuto Amwadzidzidzi
Lolani kuti ena akuthandizeni.