Pitani ku nkhani yake

Banja

Zimene Zingakuthandizeni Kuti Muzisangalala

Muzidalira Kwambiri Mulungu

Kudzifunsa mafunso awiri okha kungathandize kuti banja lanu liziyenda bwino.

Nzeru Zothandiza Kukhala Ndi Banja Losangalala

Kodi amuna, akazi, makolo komanso ana angatani kuti azisangalala m’banja?

Kuti Banja Liziyenda Bwino​—Kuchita Zinthu Mogwirizana

Kodi inuyo ndi mwamuna kapena mkazi wanu mumangokhala ngati anthu okhalira limodzi basi?

Mungatani Kuti Banja Lanu Lizisangalala: Muzisonyezana Ulemu

Baibulo lingakuthandizeni kuti muyambe kulemekezana m’banja lanu ngakhale kuti poyamba simunkalemekezana.

Muzikhala Okhulupirika

Kuti munthu akhale wokhulupirika m’banja ayenera kupewa chigololo komanso zinthu zina.

Mavuto Komanso Njira Zowathetsera

Zimene Mungachite Kuti Muzigwirizana ndi Achibale

N’zotheka kulemekeza makolo anu popanda kusokoneza banja lanu.

Kuti Banja Liziyenda Bwino​—Kukhululukirana

Kodi mungatani kuti musamaganizire kwambiri zimene mwamuna kapena mkazi wanu amalakwitsa?

Mukakumana ndi Mavuto Amwadzidzidzi

Lolani kuti ena akuthandizeni.