Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kuwerenga Komanso Kuphunzira Baibulo

Kuwerenga Baibulo

Kodi Ubwino Wowerenga Baibulo Ndi Wotani?

Kodi anthu ambiri apindula bwanji ndi kuwerenga Baibulo?

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 1: Kuganizira Mozama Mfundo za M’baibulo

Tiyerekeze kuti mwaona chikwama cha ndalama chomwe chikuoneka kuti ndi chakalekale, kodi simungakhale ndi chidwi kuti muone zimene zili mkatimo? Baibulo lili ngati chikwama choterocho. Mumapezeka mfundo zambiri zothandiza.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 2: Zimene Mungachite Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzikusangalatsani

Zinthu 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muziona zimene mukuwerenga m’Baibulo kuti ndi zenizeni.