Pitani ku nkhani yake

Moyo Komanso Imfa

Moyo

Kodi Cholinga cha Moyo N’chiyani?

Kodi munayamba mwaganizirapo funso lakuti, ‘Kodi cholinga cha moyo n’chiyani?’ Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena pa nkhaniyi.

Imfa

Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?

Kodi Baibulo limapereka malangizo otani kwa munthu amene akufuna kudzipha?

Kumwamba Komanso Kuwotcha Anthu Pamoto

Kodi Ndi Ndani Amene Amapita Kumwamba?

Anthu ambiri amaganiza kuti anthu onse abwino amapita kumwamba. Koma kodi Baibulo limaphunzitsa chiyani pa nkhaniyi?

Kodi Zinyama Zimapita Kumwamba?

Baibulo siliphunzitsa kuti ziweto kapena agalu, zidzapita kumwamba

Akufa Adzauka

Kodi Mawu Akuti Kuuka kwa Akufa Amatanthauza Chiyani?

Mungadabwe mutadziwa zimene Baibulo limanena zokhudza anthu amene adzaukitsidwe.