Pitani ku nkhani yake

Yesu

KODI YESU NDANI?

N’chifukwa Chiyani Baibulo Limati Yesu Ndi Mwana wa Mulungu?

Ngati Mulungu sanabereke Yesu ngati mmene anthu amachitira, n’chifukwa chiyani Baibulo limati Yesu ndi Mwana wa Mulungu?

Kodi Mikayeli Mkulu wa Angelo Ndi Ndani?

Amadziwika ndi dzina lina limene mumalidziwa bwino.

Yesu ali Padziko Lapansi

Kodi “Anzeru a Kum’mawa” Anali Ndani? Kodi Mulungu Ndi Amene Anawachititsa Kuti Alondole Nyenyezi ya ku Betelehemu?

Miyambo yambiri yomwe imachitika yokhudza Khirisimasi siipezeka n’komwe m’Baibulo.

Kodi Yesu Ankaoneka Bwanji?

Mfundo zina zimene Baibulo limafotokoza zimatithandiza kudziwa mmene Yesu ankaonekera.

Udindo wa Yesu Pokwaniritsa Cholinga cha Mulungu

Kodi Yesu Amatipulumutsa Bwanji?

N’chifukwa chiyani Yesu amafunika kuchonderera m’malo mwathu? Kodi kungokhulupirira Yesu n’kokwanira kuti tidzapulumuke?

Kodi Nsembe ya Yesu Imawombola Bwanji “Anthu Ambiri”?

Kodi dipo limawombola bwanji anthu ku uchimo?