Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kukhala Bwino Ndi Anthu

Kulankhulana Pazipangizo Zamakono

Muzichita Zinthu Mosamala Mukamacheza ndi Anzanu pa Intaneti

Chitani zinthu mosamala mukamacheza ndi anzanu pa Intaneti.

Kupeza Komanso Kukhala pa Chibwenzi

Kodi Ndi Chikondi Chenicheni Kapena Kungotengeka Maganizo?

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe tanthauzo la kutengeka maganizo ndiponso chikondi chenicheni.

Kodi Baibulo Limavomereza Kuti Mwamuna ndi Mkazi Azikhalira Limodzi Asanakwatirane?

Malangizo ochokera kwa Mulungu amatithandiza kudziwa zimene tingachite kuti tikhale ndi banja logwirizana ndipo anthu amene amatsatira mfundo zake zinthu zimawayendera bwino nthawi zonse.

Prejudice and Discrimination

Kodi Tingathetse Bwanji Chidani?​—Muziyesetsa Kupewa Tsankho

Chotsani kamtima koipidwa ndi anthu ena, potengera chitsanzo cha Yehova yemwe ndi wopanda tsankho.