Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kupirira Mavuto Aakulu

Kuvutika

N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Anthu Azivutika?

Anthu ambiri amafuna kudziwa kuti n’chifukwa chiyani padzikoli pali mavuto ambiri. Baibulo limapereka yankho logwira mtima pa nkhaniyi.

Imfa ya Munthu Amene Timakonda

Zimene Mungachite Mukaferedwa

Muone zinthu zimene zingakuthandizeni kupirira.

Ngozi Zadzidzidzi

Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani ya Ngozi Zadzidzidzi?

Kodi ngozi zadzidzidzi ndi chilango chochokera kwa Mulungu? Kodi Mulungu amathandiza bwanji anthu amene akhudzidwa ndi ngozi zadzidzidzi?