Moyo Wanthanzi
Kupilira Matenda
Kodi Baibulo Lingandithandize Kupirira Matenda?
Inde. Onani mfundo zitatu zimene zingakuthandizeni kuti mupirire matenda.
Mmene Mungathandizire Amene Akudwala Matenda Amaganizo
Kuthandiza mnzanu yemwe akuvutika ndi matenda amaganizo kungasinthe zinthu pa moyo wake.
Kusamalira Ena
Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yosamalira Makolo Achikulire?
Baibulo limafotokoza zimene amuna ndi akazi ena anachita m’mbuyomo posamalira makolo awo achikulire. Lilinso ndi mfundo zomwe zingathandize anthu omwe akusamalira makolo achikulire panopa.
Nkhawa
Achinyamata Ambiri Akuvutika Ndi Matenda Amaganizo—Kodi Baibulo Limanena Zotani?
Baibulo limapereka malangizo othandiza kwa achinyamata omwe akuvutika maganizo.
Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?
Kodi Baibulo limapereka malangizo otani kwa munthu amene akufuna kudzipha?
Nkhawa
Zimene Mungachite Ngati Muli Nokhanokha
Mukamamva kuti muli nokhanokha, mungayambe kuona kuti simungathe kupeza chiyembekezo, chimwemwe komanso kukhala wokhutira—komatu si choncho.