Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Moyo Wanthanzi

Kupilira Matenda

Kodi Baibulo Lingandithandize Kupirira Matenda?

Inde. Onani mfundo zitatu zimene zingakuthandizeni kuti mupirire matenda.

Mmene Mungathandizire Amene Akudwala Matenda Amaganizo

Kuthandiza mnzanu yemwe akuvutika ndi matenda amaganizo kungasinthe zinthu pa moyo wake.

Kusamalira Ena

Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yosamalira Makolo Achikulire?

Baibulo limafotokoza zimene amuna ndi akazi ena anachita m’mbuyomo posamalira makolo awo achikulire. Lilinso ndi mfundo zomwe zingathandize anthu omwe akusamalira makolo achikulire panopa.

Nkhawa

Achinyamata Ambiri Akuvutika Ndi Matenda Amaganizo—Kodi Baibulo Limanena Zotani?

Baibulo limapereka malangizo othandiza kwa achinyamata omwe akuvutika maganizo.

Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?

Kodi Baibulo limapereka malangizo otani kwa munthu amene akufuna kudzipha?

Nkhawa

Zimene Mungachite Ngati Muli Nokhanokha

Mukamamva kuti muli nokhanokha, mungayambe kuona kuti simungathe kupeza chiyembekezo, chimwemwe komanso kukhala wokhutira​—komatu si choncho.