Zizolowezi Komanso Makhalidwe Oipa
Fodya, Mankhwala Osokoneza Bongo ndi Mowa
Kodi Baibulo Limanena Kuti Kumwa Mowa Ndi Tchimo?
Baibulo limasonyeza kuti mowa ukhoza kuthandiza munthu amene akudwala m’mimba komanso likhoza kuthandiza munthu kuti azisangalala.
Kufalitsa Nkhani Pazipangizo Zamakono
Kodi Zipangizo Zanu Zimakulamulirani Kapena Mumazilamulira?
Masiku ano anthu ambiri akugwiritsa ntchito zipangizo zamakono, koma musamalole kuti zimenezi zizilamulira moyo wanu. Nanga mungadziwe bwanji kuti mwayamba kukonda kwambiri zipangizo zanu? Ngati mulidi ndi vuto limeneli kodi mungatani kuti mulithetse?
Juga
Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani ya Kutchova Juga
Kodi ndi masewera osangalatsa chabe?
Zolaula
Kodi Kuonera Zolaula Kuli Ndi Mavuto Otani?
Kodi kuonera zolaula kumakhudza bwanji anthu komanso mabanja?