Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Zizolowezi Komanso Makhalidwe Oipa

Fodya, Mankhwala Osokoneza Bongo ndi Mowa

Kodi Baibulo Limanena Kuti Kumwa Mowa Ndi Tchimo?

Baibulo limasonyeza kuti mowa ukhoza kuthandiza munthu amene akudwala m’mimba komanso likhoza kuthandiza munthu kuti azisangalala.

Kufalitsa Nkhani Pazipangizo Zamakono

Kodi Zipangizo Zanu Zimakulamulirani Kapena Mumazilamulira?

Masiku ano anthu ambiri akugwiritsa ntchito zipangizo zamakono, koma musamalole kuti zimenezi zizilamulira moyo wanu. Nanga mungadziwe bwanji kuti mwayamba kukonda kwambiri zipangizo zanu? Ngati mulidi ndi vuto limeneli kodi mungatani kuti mulithetse?

Juga

Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani ya Kutchova Juga

Kodi ndi masewera osangalatsa chabe?

Zolaula

Kodi Kuonera Zolaula Kuli Ndi Mavuto Otani?

Kodi kuonera zolaula kumakhudza bwanji anthu komanso mabanja?