Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kodi Zamoyo Zinachita Kusintha Kapena Zinalengedwa?

Zimene Baibulo Limatiuza Zokhudza Mlengi

Kodi zomwe Baibulo limanena zimagwirizana ndi zimene asayansi apeza?

Kodi Mulungu Anasintha Zamoyo Zina Polenga Mitundu Inanso ya Zamoyo?

Baibulo silitsutsa zimene asayansi amanena zoti mitundu ya zamoyo imatulutsanso zamoyo zina zofanana ndi zamtundu womwewo.

Achinyamata Ena Akufotokoza Zokhudza Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu

M’vidiyo ya maminitsi atatuyi, achinyamata akufotokoza chifukwa chake amakhulupirira kuti kuli Mulungu.